Main pages

Surah Abundance [Al-Kauther] in Chewa

Surah Abundance [Al-Kauther] Ayah 3 Location Makkah Number 108

إِنَّآ أَعْطَيْنَٰكَ ٱلْكَوْثَرَ ﴿1﴾

Ndithu takupatsa zabwino zambiri (zina mwa izo ndi mtsinje wotchedwa Kauthar).[490]

فَصَلِّ لِرَبِّكَ وَٱنْحَرْ ﴿2﴾

(Pakuti ndakupatsa zimenezo), pitiriza kupembedza Mbuye wako (moyera mtima) ndipo ipha nsembe yako (chifukwa chakuthokoza Allah pa zimene wakupatsa, monga ulemelero ndikukusankhira zabwino zambiri).[491]

إِنَّ شَانِئَكَ هُوَ ٱلْأَبْتَرُ ﴿3﴾

Ndithu mdani wako ndiye ali wopanda mwawi. [492]