Settings
Surah Abundance [Al-Kauther] in Chewa
Surah Abundance [Al-Kauther] Ayah 3 Location Makkah Number 108
إِنَّآ أَعْطَيْنَٰكَ ٱلْكَوْثَرَ ﴿1﴾
Ndithu takupatsa zabwino zambiri (zina mwa izo ndi mtsinje wotchedwa Kauthar).[490]
فَصَلِّ لِرَبِّكَ وَٱنْحَرْ ﴿2﴾
(Pakuti ndakupatsa zimenezo), pitiriza kupembedza Mbuye wako (moyera mtima) ndipo ipha nsembe yako (chifukwa chakuthokoza Allah pa zimene wakupatsa, monga ulemelero ndikukusankhira zabwino zambiri).[491]
إِنَّ شَانِئَكَ هُوَ ٱلْأَبْتَرُ ﴿3﴾
Ndithu mdani wako ndiye ali wopanda mwawi. [492]