Settings
Surah The Disbelievers [Al-Kafiroon] in Chewa
قُلۡ یَـٰۤأَیُّهَا ٱلۡكَـٰفِرُونَ ﴿1﴾
Nena (iwe Mtumiki) (s.a.w): E inu anthu osakhulupirira![493]
لَاۤ أَعۡبُدُ مَا تَعۡبُدُونَ ﴿2﴾
Sindipembedza chimene inu mukuchipembedza (kusiya Allah).
وَلَاۤ أَنتُمۡ عَـٰبِدُونَ مَاۤ أَعۡبُدُ ﴿3﴾
Inunso simumpembedza amene ine ndikumpembedza (yemwe ndi Allah).
وَلَاۤ أَنَا۠ عَابِدࣱ مَّا عَبَدتُّمۡ ﴿4﴾
Ndiponso ine sindidzapembedza chimene inu mwakhala mukuchipembedza (chifukwa inu ndinu ophatikiza Allah ndi zinthu zina).
وَلَاۤ أَنتُمۡ عَـٰبِدُونَ مَاۤ أَعۡبُدُ ﴿5﴾
Ndipo inu simudzampembedza amene ine ndikumpembedza (yemwe ndi Allah).
لَكُمۡ دِینُكُمۡ وَلِیَ دِینِ ﴿6﴾
Inu muli ndi chipembedzo chanu (chimene mukuchikhulupirira), inenso ndili ndi chipembedzo changa (chimene Allah wandisankhira).
English
Chinese
Spanish
Portuguese
Russian
Japanese
French
German
Italian
Hindi
Korean
Indonesian
Bengali
Albanian
Bosnian
Dutch
Malayalam
Romanian