Settings
Surah The mankind [An-Nas] in Chewa
Surah The mankind [An-Nas] Ayah 6 Location Makkah Number 114
قُلْ أَعُوذُ بِرَبِّ ٱلنَّاسِ ﴿1﴾
Nena: “Ndikudzitchinjiriza ndi Mbuye (Mleri) wa anthu (Yemwe akulinganiza zinthu zawo).[503]
مَلِكِ ٱلنَّاسِ ﴿2﴾
Mfumu ya anthu ( Imene iri ndi mphamvu yochita chirichonse pa iwo).
إِلَٰهِ ٱلنَّاسِ ﴿3﴾
Wopembedzedwa wa anthu.
مِن شَرِّ ٱلْوَسْوَاسِ ٱلْخَنَّاسِ ﴿4﴾
Kuzoipa za mnong’onezi (yemwe amathira unong’onezi wake m’mitimaya anthu) yemwenso amabisala (posiya unong’onezi wake ngati mwini mtimawo atankumbukira Allah).[504]
ٱلَّذِى يُوَسْوِسُ فِى صُدُورِ ٱلنَّاسِ ﴿5﴾
Yemwe amanong’oneza mzifuwa za anthu.
مِنَ ٱلْجِنَّةِ وَٱلنَّاسِ ﴿6﴾
Wochokera m’ziwanda ndi mwa anthu.”[505]